Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Danieli 2:9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma mukapanda kundidziwitsa lotoli, mlandu wanu ndi umodzi; popeza mwapanganiranatu mau onama ndi oipa, kuwanena pamaso panga, mpaka idzasanduka nyengo; cifukwa cace mundifotokozere lotoli, momwemo ndidzadziwa kuti mudzandidziwitsa kumasulira kwace komwe.

Werengani mutu wathunthu Danieli 2

Onani Danieli 2:9 nkhani