Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Danieli 11:7 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma apo pophukira mizu yace adzauka wina m'malo mwace, ndiye adzafika kulimbana nalo khamu la nkhondo, nadzalowa m'linga la mfumu ya kumpoto, nadzacita molimbana nao, nadzawalaka;

Werengani mutu wathunthu Danieli 11

Onani Danieli 11:7 nkhani