Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Danieli 11:6 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo pakutha zaka adzaphatikizana iwo; ndi mwana wamkazi wa mfumu ya kumwela adzafika kwa mfumu ya kumpoto, kupangana naye zoyenera koma mkaziyo sadzaisunga mphamvu ya dzanja lace; ngakhale mwamunayo sadzaimika, ngakhale dzanja lace; koma mkaziyo adzaperekedwa, pamodzi ndi iwo adadza naye, ndi iye amene anambala, ndi iye amene anamlimbitsa nthawi zija.

Werengani mutu wathunthu Danieli 11

Onani Danieli 11:6 nkhani