Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Danieli 10:9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo ndinamva kunena kwa mau ace, ndipo pamene ndinamva kunena kwa mau ace ndinagwidwa ndi tulo tatikuru pankhope panga, nkhope yanga pansi.

Werengani mutu wathunthu Danieli 10

Onani Danieli 10:9 nkhani