Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Danieli 10:12 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pamenepo anati kwa ine, Usaope Danieli; pakuti kuyambira tsiku loyamba lija unaika mtima wako kuzindikira ndi kudzicepetsa pamaso pa Mulungu wako, mau ako anamveka; ndipo ndadzera mau ako,

Werengani mutu wathunthu Danieli 10

Onani Danieli 10:12 nkhani