Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Samueli 9:7 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Davide ananena naye, Usaopa, pakuti zoonadi ndidzakucitira kukoma mtima cifukwa ca Jonatani atate wako; ndi minda yonse ya Sauli ndidzakubwezera, ndipo udzadya pa gome langa cikhalire.

Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 9

Onani 2 Samueli 9:7 nkhani