Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Samueli 9:6 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Mefiboseti mwana wa Jonatani, mwana wa Sauli, anafika kwa Davide, nagwa nkhope yace pansi, namlambira. Ndipo Davide anati, Mefiboseti! Nayankha iye, Ndine mnyamata wanu.

Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 9

Onani 2 Samueli 9:6 nkhani