Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Samueli 7:7 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

M'malo monse ndinayendamo limodzi ndi ana onse a Israyeli kodi ndinanena ndi pfuko limodzi la Aisrayeli, limene ndinalamulira kudyetsa anthu anga Aisrayeli, kuti, Munalekeranji kundimangira nyumba yamikungudza?

Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 7

Onani 2 Samueli 7:7 nkhani