Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Samueli 7:12 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pamene masiku ako akadzakwaniridwa, ndipo iwe udzagona ndi makolo ako, Ine ndidzaukitsa mbeu yako pambuyo pako, imene idzaturuka m'matumbo mwako, ndipo ndidzakhazikitsa ufumu wace.

Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 7

Onani 2 Samueli 7:12 nkhani