Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Samueli 5:6 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo mfumu ndi anthu ace anamuka ku Yerusalemu kuyambana nao Ajebusi, nzika za dziko; ndiwo ananena kwa Davide ndi kuti, Sudzalowa muno, koma akhungu ndi opunduka adzakupitikitsa; ndiko kunena kuti, Davide sakhoza kulowa muno.

Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 5

Onani 2 Samueli 5:6 nkhani