Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Samueli 5:5 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ku Hebroni anacita ufumu pa Yuda zaka zisanu ndi ziwiri kudza miyezi isanu ndi umodzi; ndi ku Yerusalemu anacita ufumu pa Aisrayelionse ndi Ayuda omwe zaka makumi atatu mphambu zitatu.

Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 5

Onani 2 Samueli 5:5 nkhani