Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Samueli 5:2 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Masiku anapitawo, pamene Sauli anali mfumu yathu, inu ndinu amene munatsogolera Aisrayeli kuturuka nao ndi kubwera nao; ndipo Yehova ananena nanu, Uzidyetsa anthu anga Israyeli, ndi kukhala mtsogoleri wa Israyeli,

Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 5

Onani 2 Samueli 5:2 nkhani