Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Samueli 4:12 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Davide analamulira anyamata ace, iwo nawapha, nawapacika m'mbali mwa thamanda ku Hebroni atawadula manja ndi mapazi ao. Koma mutu wa Isiboseti anautenga nauika m'manda a Abineri ku Hebroni.

Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 4

Onani 2 Samueli 4:12 nkhani