Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Samueli 3:19 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Abineri analankhulanso m'kumva kwa Abenjamini; Abineri anamukanso ku Hebroni kulankhula m'makutu a Davide zonse zakukomera Aisrayeli ndi a nyumba yonse ya Benjamini.

Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 3

Onani 2 Samueli 3:19 nkhani