Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Samueli 3:14 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Davide anatumiza mithenga kwa Isiboseti mwana wa Sauli, nati, Undipatse mkazi wanga Mikala amene ndinadzitomera ndi nsonga za makungu za Afilisti zana limodzi.

Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 3

Onani 2 Samueli 3:14 nkhani