Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Samueli 24:4 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma mau a mfumu anapambana Yoabu ndi atsogoleri a khamulo. Ndipo Yoabu ndi atsogoleri a khamulo anaturuka pamaso pa mfumu kuti akawerenge anthu a Israyeli.

Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 24

Onani 2 Samueli 24:4 nkhani