Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Samueli 24:21 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Arauna nati, Mbuye wanga mfumu, mwadzeranji kwa mnyamata wanu? Ndipo Davide anati, Kugula dwale lako gi, kuti ndimangirepo Yehova guwa lansembe, kuti mliriwo ulekeke kwa anthu.

Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 24

Onani 2 Samueli 24:21 nkhani