Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Samueli 24:16 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo pamene mthenga anatambasulira dzanja lace ku Yerusalemu kuuononga, coipaco cinacititsa Yehova cisoni, iye nauza mthenga wakuononga anthuwo, kuti, Kwafikira tsopano, bweza dzanja lako. Ndipo mthenga wa Yehova anali pa dwale la Arauna Mjebusi.

Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 24

Onani 2 Samueli 24:16 nkhani