Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Samueli 23:21 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

ndipo anapha M-aigupto munthu wokongola, M-aigupto anali nao mkondo m'dzanja lace; koma iyeyo anatsikira kwa iye ndi ndodo, nasolola mkondowo m'dzanja la M-aigupto, namupha ndi mkondo wa iye mwini.

Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 23

Onani 2 Samueli 23:21 nkhani