Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Samueli 23:20 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Benaya, mwana wa Yehoyada, mwana wa ngwazi wa ku Kabzeli amene anacita zamphamvu; iye anapha anthu awiri a Moabu akunga mikango, natsikanso iye napha mkango m'mbuna nyengo ya cipale cofewa;

Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 23

Onani 2 Samueli 23:20 nkhani