Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Samueli 21:7 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma mfumu inaleka Mefiboseti mwana wa Jonatani, mwana wa Sauli, cifukwa ca lumbiro la kwa Yehova linali pakati pa Davide ndi Jonatani mwana wa Sauli.

Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 21

Onani 2 Samueli 21:7 nkhani