Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Samueli 20:7 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anaturuka namtsata anthu a Yoabu, ndi Akereti ndi Apeleti, ndi anthu onseamphamvu; naturuka m'Yerusalemu kukalondola Seba mwana wa Bikri.

Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 20

Onani 2 Samueli 20:7 nkhani