Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Samueli 20:2 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Comweco anthu onse a Israyeli analeka kutsata Davide, natsata Seba mwana wa Bikri; koma anthu a Yuda anaphatikizana ndi mfumu yao, kuyambira ku Yordano kufikira ku Yerusalemu.

Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 20

Onani 2 Samueli 20:2 nkhani