Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Samueli 18:9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Abisalomu anakomana ndi anyamata a Davide. Abisalomu naberekeka pa nyuru yace, ndipo nyuruyo inapita pansi pa nthambi zolimba za thundu wamkuru. Ndipo mutu wace unakodwa ndi mtengo, iye ali lende pakati pa thambo ndi pansi ndi nyuru imene inali pansi pa iye Inapitirira.

Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 18

Onani 2 Samueli 18:9 nkhani