Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Samueli 18:8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pakuti nkhondo inatanda pa dziko lonse, ndipo tsiku lomwelo nkhalango inaononga anthu akuposa amene anaonongeka ndi lupanga.

Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 18

Onani 2 Samueli 18:8 nkhani