Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Samueli 18:17 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anatenga Abisalomu namponya m'cidzenje cacikuru kunkhalangoko; naunjika pamwamba pace mulu waukuru ndithu wamiyala; ndipo Aisrayeli onse anathawa yense ku hema wace.

Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 18

Onani 2 Samueli 18:17 nkhani