Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Samueli 17:28-29 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

28. iwo anabwera nao makama, ndi mbale, ndi zotengera zadothi, ndi tirigu, ndi barele, ndi ufa, ndi tirigu wokazinga, ndi nyemba, ndi mphodza, ndi zokazinga zina,

29. ndi uci ndi mafuta, ndi nkhosa, ndi mase a ng'ombe, kutiadye Davide, ndi anthu amene anali naye; pakuti anati, Anthu ali ndi njala, olema, ndi aludzu m'cipululumo.

Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 17