Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Samueli 17:27 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo kunali pakufika Davide ku Mahanaimu, Sobi mwana wa Nahasi wa ku Raba wa ana a Amoni, ndi Makiri mwana wa Amiyeli wa ku Lodebara, ndi Barizilai Mgileadi wa ku Rogelimu,

Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 17

Onani 2 Samueli 17:27 nkhani