Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Samueli 17:17 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Jonatani ndi Ahimaazi anakhala ku Enirogeli; mdzakazi adafopita kuwauza; ndipo iwo anapita nauza mfumu Davide, pakuti sangaoneke iwowo alikulowa m'mudzi.

Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 17

Onani 2 Samueli 17:17 nkhani