Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Samueli 16:8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Yehova wabwezera pa iwe mwazi wonse wa nyumba ya Sauli, amene iwe wakhala mfumu m'malo mwace; ndipo Yehova wapereka ufumuwo m'dzanja la Abisalomu mwana wako; ndipo ona, wagwidwa m'kuipa kwako kwa iwe wekha, cifukwa uli munthu wa mwazi.

Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 16

Onani 2 Samueli 16:8 nkhani