Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Samueli 16:3 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo mfumu inati, Mwana wa mbuye wako ali kuti? Ziba nanena ndi mfumu, Onani, akhala ku Yerusalemu; pakuti anati, Lero nyumba ya Israyeli idzandibwezera ufumu wa atate wanga.

Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 16

Onani 2 Samueli 16:3 nkhani