Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Samueli 14:16 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pakuti mfumu idzamvera ndi kupulumutsa mdzakazi wace m'dzanja la munthu wakufuna kundiononga ine pamodzi ndi mwana wanga, kuticotsa ku colowa ca Mulungu.

Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 14

Onani 2 Samueli 14:16 nkhani