Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Samueli 14:14 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pakuti kufa tidzafa, ndipo tiri ngati madzi otayika pansi amene sakhoza kuwaolanso; ngakhale Mulungu sacotsa moyo, koma alingalira ngra yakuti wotayikayo asakhale womtayikira iye.

Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 14

Onani 2 Samueli 14:14 nkhani