Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Samueli 13:4 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Nanena naye, Iwe mwana wa mfumu, uonderanji tsiku ndi tsiku? Sungandiuze kodi? Ndipo Amnoni anati kwa iye, Ndikonda Tamara, mlongo wa mbale wanga Abisalomu.

Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 13

Onani 2 Samueli 13:4 nkhani