Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Samueli 13:3 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma Amnoni anali ndi bwenzi lace, dzina lace ndiye Jonadabu, mwana wa Sineya, mbale wa Davide. Ndipo Jonadabu anali munthu wocenjera ndithu.

Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 13

Onani 2 Samueli 13:3 nkhani