Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Samueli 13:33 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Cifukwa cace tsono mfumu mbuye wanga asasauke mtima ndi cinthuci, ndi kuganiza kuti ana amuna onse a mfumu afa; pakuti Amnoni yekha wafa.

Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 13

Onani 2 Samueli 13:33 nkhani