Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Samueli 12:30 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Nacotsa korona pa mutu wa mfumu yao; kulemera kwace kunali talente wa golidi; ndipo m'menemo munali miyala ya mtengo wapatali; ndipo anamuika pa mutu wa Davide. Iye naturutsa zofunkha za mudziwo zambirimbiri.

Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 12

Onani 2 Samueli 12:30 nkhani