Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Samueli 11:11 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Uriya nanena ndi Davide, Likasalo, ndi Israyeli, ndi Yuda, alikukhala m'misasa, ndi mbuye wanga Yoahu, ndi anyamata a mbuye wanga alikugona kuthengo, potero ndikapita ine kodi ku nyumba yanga kuti ndidye, ndimwe, ndigone ndi mkazi wanga? Pali inu, pali moyo wanu, sindidzacita cinthuci.

Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 11

Onani 2 Samueli 11:11 nkhani