Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Samueli 10:3 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma akalonga a ana a Amoni anati kwa Hanuni mbuye wao, Kodi muganiza kuti Davide alemekeza atate wanu, popeza anakutumizirani osangalatsa? Kodi Davide sanatumiza anyamata ace kwa inu, kuti ayang'ane mudziwo ndi kuuzonda ndi kuupasula?

Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 10

Onani 2 Samueli 10:3 nkhani