Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mbiri 7:8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Nthawi yomweyo Solomo anacita madyerero masiku asanu ndi awiri, ndi Aisrayeli onse pamodzi naye, khamu lalikuru ndithu, kuyambira polowera ku Hamati kufikira mtsinje wa ku Aigupto.

Werengani mutu wathunthu 2 Mbiri 7

Onani 2 Mbiri 7:8 nkhani