Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mbiri 6:41 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo tsopano nyamukani, Yehova Mulungu, kudza kopumulira kwanu, Inu ndi likasa la mphamvu yanu; ansembe anu, Yehova Mulungu, abvale cipulumutso; ndi okondedwa anu akondwere nazo zabwino.

Werengani mutu wathunthu 2 Mbiri 6

Onani 2 Mbiri 6:41 nkhani