Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mbiri 36:4 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndi mfumu ya Aigupto anamlonga Eliyakimu mng'ono wace mfumu ya Yuda ndi Yerusalemu, nasintha dzina lace likhale Yehoyakimu. Koma Neko anatenga Yehoahazi mkuru wace, namuka naye ku Aigupto.

Werengani mutu wathunthu 2 Mbiri 36

Onani 2 Mbiri 36:4 nkhani