Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mbiri 34:3 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pakuti atakhala mfumu zaka zisanu ndi ziwiri akali mnyamata, anayamba kufuna Mulungu wa Davide kholo lace; ndipo atakhala zaka khumi ndi cimodzi anayamba kuyeretsa Yuda ndi Yerusalemu, kuzicotsa misanje, ndi zifanizo, ndi mafano osema, ndi mafano oyenga,

Werengani mutu wathunthu 2 Mbiri 34

Onani 2 Mbiri 34:3 nkhani