Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mbiri 34:13 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Anayang'aniranso osenza akatundu, nafulumiza onse akugwira nchito ya utumiki uli wonse; ndi mwa Alevi munali alembi, ndi akapitao, ndi odikira.

Werengani mutu wathunthu 2 Mbiri 34

Onani 2 Mbiri 34:13 nkhani