Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mbiri 31:5 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo pobuka mau aja, ana a Israyeli anapereka mocuruka, zobala zoyamba za tirigu, vinyo, ndi mafuta, ndi uci, ndi za zipatso zonse za m'minda, ndi limodzi la magawo khumi la zonse anabwera nazo mocuruka.

Werengani mutu wathunthu 2 Mbiri 31

Onani 2 Mbiri 31:5 nkhani