Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mbiri 29:25 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anaika Alevi m'nyumba ya Yehova ndi nsanje, ndi zisakasa, ndi azeze, monga umo adauzira Davide, ndi Gadi mlauli wa mfumu, ndi Natani mneneriyo; pakuti lamulo ili lidafuma kwa Yehova mwa aneneri ace.

Werengani mutu wathunthu 2 Mbiri 29

Onani 2 Mbiri 29:25 nkhani