Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mbiri 27:5 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Anayambananso ndi mfumu ya ana a Amoni, namgonjetsa, Ndi ana a Amoni anamninkha caka comweci matalente a siliva zana limodzi, ndi miyeso ya tirigu zikwi khumi, ndi ya barele zikwi khumi. Ana a Amoni anabwera nazo zomwezo kwa iye caka caciwiri ndi cacitatu comwe.

Werengani mutu wathunthu 2 Mbiri 27

Onani 2 Mbiri 27:5 nkhani