Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mbiri 25:19 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Mukuti, Taonani, ndakantha Aedomu, nukwezeka mtima wanu kudzikuza; khalani kwanu tsopano, mungadziutsire tsoka, mungagwe, inu, ndi Yuda pamodzi ndi inu.

Werengani mutu wathunthu 2 Mbiri 25

Onani 2 Mbiri 25:19 nkhani