Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mbiri 24:13 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Momwemo anacita ogwira nchito, nikula nchito mwa dzanja lao, nakhazikitsa iwo nyumba ya Mulungu monga mwa maonekedwe ace, nailimbitsa.

Werengani mutu wathunthu 2 Mbiri 24

Onani 2 Mbiri 24:13 nkhani