Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mbiri 24:11 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo kunali, pamene amabwera nalo bokosi alipenye mfumu, mwa manja a Alevi, nakapenya kuti ndalama zinacurukamo, amadza mlembi wa mfumu, ndi kapitao wa wansembe wamkulu, nakhutula za m'bokosi, nalisenza ndi kubwera nalo kumalo kwace. Anatero tsiku ndi tsiku, nasonkhanitsa ndalama zocuruka.

Werengani mutu wathunthu 2 Mbiri 24

Onani 2 Mbiri 24:11 nkhani